Loading...

Download
  • Genre:Others
  • Year of Release:2024

Lyrics

Mmmmmmh ooooooh ooooooh Akuzike Thawe yeahhhhhhhhh eeh eeh


Pa tsiku lachitatu panali ukwati ku Kana wa ku Galileya

Amayi a Yesu anali komweko, ndipo Yesu ndi ophunzila ake anaitanidwa Vinyo atatha, a make a Yesu ananena kwa Iye "Alibe vinyo"


Nthawi inali itakwana, kuti Yesu awulule

Ulemelelo wake ndi mphamvu zake, m'njira yodabwitsa kumva Vinyo anatha, koma Yesu anali atangoyamba kumene Kuti awonetse ulemelelo Wake, kwa aliyense


Aleluya, Yesu ndiye amene asandutsa madzi kukhala vinyo

Aleluya, Iye ndi Mfumu ya mafumu, amene ali wamphamvu ndi Waumulungu

Aleluya, ulemerero Wake wawululidwa, mu chizindikilo chozizwitsa ichi


Yesu anati kwa iye, Mkazi, ichi chiri chotani ndi Ine?

Nthawi yanga sinafike"

Amake adanena kwa atumiki, Chitani chilichonse chimene angakuuzeni.

Kumeneko kunali mitsuko yamadzi isanu ndi umodzi yochitira mwambo wachiyeretso wa Ayuda


Nthawi inali itakwana, kuti Yesu awulule

Ulemelelo wake ndi mphamvu zake, m'njila yodabwitsa kumva

Vinyo anatha, koma Yesu anali atangoyamba kumene

Kuti awonetse ulemerero Wake, kwa aliyense


Aleluya, Yesu ndiye amene asandutsa madzi kukhala vinyo

Aleluya, Iye ndi Mfumu ya mafumu, amene ali wamphamvu ndi Wa umulungu

Aleluya, ulemelelo Wake wawululidwa, mu chizindikilo chozizwitsa ichi


Yesu anati kwa antchito, Dzazani mitsukoyo ndi madzi.

Ndipo adazidzaza mpaka pamlomo

Ndipo anati kwa iwo, Tulani tsopano, mupite nayo kwa mkulu wa phwando.

Chotero anamtengera kwa iye, ndipo iye analawa madzi amene anasanduka vinyo


Nthawi inali itakwana, kuti Yesu awulule

Ulemelelo wake ndi mphamvu zake, m'njira yodabwitsa kumva

Vinyo anatha, koma Yesu anali atangoyamba kumene

Kuti awonetse ulemelelo Wake, kwa aliyense


Aleluya, Yesu ndiye amene asandutsa madzi kukhala vinyo

Aleluya, Iye ndi Mfumu ya mafumu, amene ali wamphamvu ndi Waumulungu

Aleluya, ulemelelo Wake wawululidwa, mu chizindikilo chozizwitsa ichi


Mkulu wa phwando adayitana mkwatiyo nanena naye "Munthu aliyense ayambe apereka vinyo wokoma, ndipo anthu akaledzera, kenako amapereka vinyo wosauka Koma iwe wasunga vinyo wabwino kufikira tsopano lino"


Mmmmmmh ooooooh ooooooh Akuzike Thawe yeahhhhhhhhh eeh eeh

+

      -   or   -

      -   or   -

      NG +234
          -You can log in via below methods-
          Reset password via e-mail
          -or-
          Reset password via e-mail
          If you have any questions, please feedback on Boomplay App or send an email to [email protected].

          Please Select A Playlist

          Add New Playlist

          Share on

          Embed: Love & Light EP

          Custom Size :

          • Default
          • Desktop(300*600)
          • Mobile(300*250)

          Type :

          • HTML/HTML5 (WordPress Supported)
          Get Boomplay Premium
          for
          Payment Method
          Pay With
            Review and pay
            Order Date
            Payment Method
            Due Today
            Flutterwave
              Subscription Successful

              Congratulations! You have successfully activated Boomplay 1 Month Premium.

              Now you have access to all the features of Boomplay App.
              Payment Failed

              Please check your balance and then try again.

              You'll lose your subscription if we don't have a working payment method for your account, so please check your payment details.
              Need help? Contact Boomplay Subscription Support.
              Payment Processing...
              10 s

              Payment is being processed by . Please wait while the order is being comfirmed.

              Payment Processing
              Your order is processing, and it may take up to a few days for the service provider to handle your payment. Please kindly stay tuned and check your order status in ‘User Center’.
              About Order Status